Nkhani
-
Imfa ya wa kabanza
Anthu okwiya m’taunishipi ya Machinjiri mu mzinda wa Blantyre aphwanya mazenera ndi zitseko za polisi yaing’ono ya Nanthoka ndi kuotcha…
Read More » -
Wakuba ufa ndi makala agamulidwa zaka 4
Bambo Cosmas Chiwambo, a zaka 22, omwe amachokera m’mudzi mwa Mwamadi kwa T/A Chikumbu m’boma la Mulanje, alamulidwa kuti akakhale…
Read More » -
Amanga oba zitsulo pa mlatho
Apolisi m’boma la Mulanje atsekera m’chitokosi abambo anayi powaganizira kuti adaba zitsulo za pa mlatho wopezeka m’dera la kummwera cha…
Read More » -
Akachasu nawo akulira ndi kukwera kwa shuga
Mwina n’kumaona ngati amene amakonda za tseketseke monga tiyi ndi makeke okha ndi amene akulira ndi kusowa komanso kukwera mtengo…
Read More » -
Kusamvana pa mwambo wokumbukira Chilima
Mwambo wokumbukira yemwe adali mtsogoleri wakale wa dziko lino a Saulos Chilima uchitika Lachiwiri likudzali kwawo ku Nsipe komwe thupi…
Read More » -
Awachotsa pa mpando atayendera a Bushiri
Kadaulo pa ndale kuno ku Malawi a George Chaima komanso wa ku South Africa a Dr Zwakala ati payenera kukhala…
Read More » -
‘Bweretsani zakudya osati Sim-card ku ndende’
Mkulu wa asilikali pa ndende ya Zomba Central Prison a Austin Nyoni ati m’malo mowotcha kapena kuphwanya ma foni ndima…
Read More » -
Mafumu alankhula pa chigamulo cha khoti pa CDF
Chigamulo cha khothi choletsa aphungu kuyendetsa ndalama zachitukuko za Constituency Development Fund (CDF) chapereka maganizo osiyana pakati pa anthu. Khoti…
Read More » -
Banja ndalilephera
Anatche, muli bwanji? Ine mavuto.Banja ndidalikondetsetsa koma ndikuona ngati ndililephera. Ndili pa banja ndipo tili ndi ana awiri. Wina wamaliza…
Read More » -
Achenjeza obwereketsa galimoto: Kuli mbanda
Bambo wina yemwe dzina lake ndi Emmanuel Davie, ali m’manja mwa apolisi pomuganizira kuti adanamiza anthu kuti ndi msilikali wa…
Read More »