Chichewa
-
Anatchereza
Akuti tibwererane Anatchereza, Mmbuyomu ndidakwatiwa, koma banja lidatha ndipo ndidapeza mwamuna wina. Banja ndi mwamuna wachiwiri uja lidathanso kaamba koti…
Read More » -
Mpofunika kuthana Ndi nyongolotsi
Kale alimi a m’gulu la ulimi wa ng’ombe la Chilangoma kwa T/A Kuntaja m’boma la Blantyre samapindula ndi ulimiwu kaamba…
Read More » -
Mbewu ya chimanga izigwirizana ndi dera
Ngakhale mbewu za makono zimabereka mochuluka ndipo zina zimacha msanga, akatswiri a zaulimi wa mbewu akuti mlimi amayenera asankhe mbewu…
Read More » -
Anatchereza
Bwenzi langa akufuna zogonana Gogo Anatchereza, Ndine mtsikana wa zaka 19 ndipo ndili pa chibwenzi ndi mnyamata wina. Koma chomwe…
Read More » -
Nkhukutembo ndi dilu
Amaweta nkhukutembo mofanana ndi nkhuku pozipatsa madeya ndi ndiwo zamasamba komanso madzi. Makola nawo ndi osasiyana ndipo zimatha kugonera m’khola…
Read More » -
Katemera wa covid ayamba
Mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera Lachinayi adalandira katemera wa matenda a Covid 19 pachipatala chapadera cha matendawa chomwe achikhazikitsa…
Read More » -
Phindu la kusankhiratu fodya pothyola
Mlimi akasankhiratu fodya wake pamene akuthyola, kusoka ndi kuumitsa, amapeza phindu lochuluka kusiyana ndi kumangomusakaniza ndi kudzasankha atamuumitsa kale. Alangizi…
Read More » -
Amwalira atathawa m’chipatala
Mayi wina wa zaka zapafupifupi 60 adamwalira maola anayi,atathawitsidwa m’chipatala cha paboma la Nkhotakota ndi abale ake, atamupeza ndi matenda…
Read More » -
Ndi ana omwe akudzipha
Bambo wina adadzipha m’boma la Chiradzulu atazindikira kuti mkazi wake amachita ubwenzi wa mseri ndi mchimwene wake. Izitu zidaululika pomwe…
Read More » -
Mfutso mpatali
Chilimwe chikuyandikira ndipo chakudya cha ziweto chili paliponse. Mkulu wa zaulimi wa ziweto m’boma la Kasungu akuti apa ndi pamene…
Read More »