Chichewa
-
Kampani yatsopano ikatamutsa alimi
Kampani yatsopano yogula ndi kugulitsa zakumunda ya Auction Holdings Limited Commodities Exchange (AHCX) yamema alimi kuti akagulitse mbewu zawo kubungweli…
Read More » -
Kugwiririra ana kudzatha?
Pafupufupi tsiku lililonse tikumamva kapena kuwerenga malipoti akuti mwana wagwiririridwa penapake. Omangidwa akumangidwa. Kugwira ndende ndiye kosakamba koma zikuoneka kuti…
Read More » -
Kupakula kukapitolo, JB achotsa nduna
Mtsogoleri wadziko lino Joyce Banda Lachitatu adakana kupumitsa mamulumuzana ena aboma kutsatira kupakula ndalama za boma kumene kwanyanya kulikulu la…
Read More » -
A ku Mozambique akulembetsa mavoti
Nzika zina za m’dziko la Mozambique zikulembetsa nawo m’kaundula wa mavoti ku Dedza popofuna kuti zidzavote nawo pa chisankho cha…
Read More » -
Banda adataya mwayi
Mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda adataya mwayi wosonyeza bwino lomwe kuti akudziwa chimene akuchita polimbana ndi chiwanda chidalowa kulikulu…
Read More » -
Mugwiliranji bere la mwini?
Masiku apitawa mtsikana wina adandifotokozera za momwe mphongo ina idagwirira bere lake pa msewu mumzinda wa Lilongwe. Mtsikanayu adali akungodziyendera …
Read More » -
Nam yapindulanji pa Tigresses?
Bungwe la Malawi National Council of Sports tsopano layeretsa timu ya Tigresses kuti Nam ndiyo yolakwa pankhani yoti timuyi ichotsedwe…
Read More » -
MW’s poetry off creative lane
The beginning in art is always good and promising, but once self-acclaimed artists detect gold in it and attempt to…
Read More » -
Papsa tonola, kusolola kwaphweka ku Kapitolo
Kwagwa papsa tonola kulikulu la dziko lino (Capital Hill) ku Lilongwe komwe akuluakulu ena ogwira ntchito zowerengera chuma cha boma…
Read More » -
‘Makuponi si yankho, ingosiyani’
Ngakhale boma lili kalikiliki ndi ndondomeko ya zipangizo zotsika mtengo, mphunzitsi wa zandale Joseph Chunga komanso mkulu woona zaufulu wachibadwidwe…
Read More »