Chichewa
-
2019: Chaka cha mbiri pa zisankho
Chaka cha 2019 chidzalowa m’mbiri ya dziko la Malawi ngati chaka chomwe atsogoleri azipani adakwekwetsana koopsa komanso koyamba mukhoti pankhani…
Read More » -
Amalawi adalankhula kudzera m’zionetsero
M’chaka chomwe chikuthachi, Amalawi adamasula thumba la ukali wawo nkulankhula mokwenza makamaka pofuna kuwonetsa kuti adazindikira za ufulu ndi udindo…
Read More » -
Mipingo yadzudzula nkhanza
Atsogoleri a mipingo ati nkhanza makamaka zochitira ana ndi amayi zanyanya m’dziko muno moti asungwana 21 pa 100 aliwonse komanso…
Read More » -
‘Zionetsero zili m’njira’
Mgwirizano wa mabungwe omenyera ufulu wa anthu wa Human Rights Defenders Coalition (HRDC) wati ukukonza mchochombe wina wa zionetsero zofuna…
Read More » -
Chipwirikiti ku Malawi
Kuphwanya ndi kusalemekeza malamulo kwayala nthenje m’dziko muno. Anthu akungopha ngati akupha nkhuku, kugwiririra, kuononga ngakhalenso kuyatsa katundu. Sabata yatha,…
Read More » -
Ayesa zida za Ebola
Patangodutsa sabata zitatu munthu wina wa m’boma la Karonga ataganiziridwa kuti ali ndi Ebola, aboma ayamba kuyesa zida zothandiza odwala…
Read More » -
Adzudzula MEC
Katswiri wa ndale wa sukulu yaukachenjede ya University of Livingstonia (Unilia), George Phiri, wati bungwe la MEC lidalakwa kuimitsa chisankho…
Read More » -
Kutentha koonjeza kuzinga maiko
A nthambi yoona za nyengo m’dziko muno auza Amalawi kuti alimbe mtima chifukwa nyengo yotentha yomwe yakhala m’dziko muno kwa…
Read More » -
Lero moto, mawa moto!
Pali mtunda kuti dziko lino likhale lodzidalira pothana ndi ngozi zamoto pamene zadziwika kuti makhonsolo m’dziko muno alibe zipangizo zokwanira…
Read More » -
Mvula yayandikira, makuponi kulibe
Pamene ndondomeko yogawa makuponi imayembekezeka kutha dzulo, Tamvani m’sabata ikuthayi idapeza kuti madera ena ndondomeko yolemba olandira komanso kugawa makuponi…
Read More »