Chichewa
-
Anatchereza
Kodi nditani? Gogo Natchereza Ndine mtsikana wa zaka 25 ndipo ndakhala pa chibwenzi ndi mnyamata wina kwa zaka zinayi. Mnyamatayu…
Read More » -
Ndidakamira kufunda nawo ambulera’
Padali pa 5 February 2014, kunja kuli mvula yamphamvu ya mabingu pomwe Devlin Nazombe kapena kuti ‘Mmisiri Wopanda Zida’ yemwe…
Read More » -
Apereka bajeti lolemba
Nduna ya zachuma Joseph Mwanamvekha alengeza ndondomeko ya chuma yomwe boma lakonza kuti ligwiritse ntchito m’chaka cha 2019/20 Lolemba pa…
Read More » -
Tetezani ana ku BP
Chimodzimodzi akulu, ana nawo amakhala pachiopsezo cha matenda othamanga magazi choncho makolo akuyenera kuwateteza, watero mkulu wa pa chipatala cha…
Read More » -
Samalani ndi chitopa
Kuchokera ku phindu la ulimi wothirira, Catherine Bamusi wa m’boma la Blantyre adaganiza zogulako nkhuku zachikuda kuti zizimupatsa manyowa, ndiwo…
Read More » -
‘Masiku 100 a Mutharika sanakome’
Mtsogoleriwa dziko lino Peter Mutharika sabata yatha adakwanitsa masiku 100 pampando wa pulezidenti koma panyengoyi sadamwe wa mkaka.. ChiulutsirenikupambanakwaMutharika, Amalawi…
Read More » -
Abwekera ulimi wa nsomba
Kuweta nsomba za mitundu yosiyana ndi kopindulitsa chifukwa ambiri amazikonda. Kwa alimi a nsomba, phindu ndiye ndi la mnanu. HOLYCE…
Read More » -
Mwapasa achoke—HRDC
Zipani za Malawi Congress Party (MCP) ndi UTM Party zati ziunika mwakuya ganizo la mgwirizano wa mabungwe omenyera ufulu wa…
Read More » -
Zionetsero zaima
Anthu zikwizikwi adabwerera manja ali m’khosi kuchoka m’malo a zionetsero Lachitatu pa 28 August 2019 atauzidwa kuti zionetserozo zalephereka kaamba…
Read More » -
Mtunda ulipo pa zokambirana
Mtsogoleri wakale wa dziko lino, Bakili Muluzi sali kutali kwenikweni ndi khumbo lake lofuna kukumana ndi atsogoleri a Human Right…
Read More »