Chichewa
-
DPP yasankha atsogoleri atsopano
Msonkhano wa masiku atatu wa chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) womwe umachitikira mu mzinda wa Blantyre wasankha mtsogoleri wa…
Read More » -
Chilima adzapikitsana nawo chaka cha mawa
Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Saulos Chilima, wati adzaima nawo pa zisankho za chaka cha mawa dongosolo lonse loyenera…
Read More » -
Kampeni yayamba ndi ukali
DPP ithamangitsa otsutsa ku Thyolo Kumeneko ndi kunyumba kwa APM—Chakale Kwa eni kulibe mkuwe. Mdima udadza masanasana m’boma la Thyolo…
Read More » -
Kalembera wa zisankho ali mkati
Dzuwa salozerana, kalembera wa zisankho udayamba Lachiwiri m’maboma a Dedza, Salima ndi Kasungu. Izitu zikudza pokonzekera chisankho cha makhansala, aphungu…
Read More » -
Ming’alu m’kalembera wa chisankho cha 2019
Pamene kalembera wa chisankho cha pa 21 May 2019 akuyamba Lachiwiri likudzali, akadaulo ena awona kale ming’alu yakudza chifukwa chokana…
Read More » -
Gulewamkulu, agumula sitolo
Gulewamkulu wina Lachwiri lapitalo akumukayikira kuti adagumula sitolo ina pamsika wa Nkhalambayasamba m’boma la Mchinji ndipo akumukaikira kuti adasakaza katundu…
Read More » -
Ntchito za wedewede zanyanya
Kusowa ndalama zoyendera zitukuko komanso kulekera anthu a kumudzi kugwira ntchito zomangamanga zachitukuko kukuchititsa kuti ntchitozi zizikhala zawedewede, atero akadaulo…
Read More » -
Chigodola chifalikira maboma ena
Matenda a chigodola amene adabuka m’maboma a Blantyre ndi Neno, ayamba kufalikiranso m’maboma ena, watero unduna wa zamalimidwe. Matendawa adayambira…
Read More » -
Apha mwana atasemphena za ndalama
Apolisi m’boma la Mangochi amanga ndi kutsekera m’chitokosi mayi wa zaka 28 chifukwa chomuganizira kuti wapha mwana wake wa zaka…
Read More » -
Afuna kudzikhweza nsanje itakula
Apolisi ya Mponela ku Dowa amanga mayi wa zaka 24 Ketrina Paulo pomuganizira kuti amafuna kudzikhweza ponyansidwa ndi mwamuna wake…
Read More »