Chichewa
-
Khama ndiye yankho poweta ng’ombe zamkaka
Kuchionetsero cha zaulimi cha National Agriculture Fair ku Trade Fair Grounds mumzinda wa Blantyre, Peacewell Edward Mlanga, wochokera kwa Senior…
Read More » -
Kusanthula khansa ya m’mawere
Petani Mtonga, wachiwiri kwa mkulu wa nthambi ya matenda a khansa kuchipatala cha Queen Elizabeth mumzinda wa Blantyre wati matenda…
Read More » -
Chisamaliro choyenera cha ng’ombe za mkaka
Ngakhale alimi ambiri a ng’ombe za mkaka amabwekera kuti akupeza phindu ku ulimiwu, Jacob Mwasinga, mlangizi wa ziweto ku Mzuzu…
Read More » -
Osauka alibe mawu
Kwa zaka 12, ena mwa omwe akuwaganizira milandu yakupha akadali pa alimandi m’ndende podikira chilungamo pa milandu yoganiziridwa…
Read More » -
Chilengedwe chikubwerera ku Mangochi
Sungapirire mfuu wa mbalame—wopokerezedwa bwino ngati nyimbo m’mitengo yachilengedwe m’boma la Mangochi. Nkhalango yachilengedwe ya m’mudzi mwa Chembe m’boma…
Read More » -
Milandu yachepa ku Blantyre
Milandu yosiyanasiyana mu mzindawa Blantyre yatsika kuchoka pa 328 mu February chaka chatha kufika pa 204 mwezi omwewo chaka…
Read More » -
Maphunziro alowa libolonje
Mphunzitsimmodzi, ana 110 Komaaphunzitsi 10 000 akusowantchito Dziko la Malawi lalephera kukwaniritsa loto lake loti pofika chaka chino, mphunzitsi mmodzi…
Read More » -
Ine ayi, Dausi wakana Chaponda
Zomwe zachitika ku bwalo la mirandu ku Lilongwe m’sabatayi zalephera kupherezera mwambi woti khoswe akakhala pa mkhate sapheka. Khwimbi…
Read More » -
Ulendo wa chisankho wapsa
Zipani zina zati bungwe loyendetsa chisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) liyenera kukwaniritsa zomwe lidalonjeza sabata yatha kuti chisankho cha…
Read More » -
Zikhulupiriro zikufalitsa kolera—unduna
Unduna wa zaumoyo wati zikhulupiriro ndizo zikuchititsa kuti chiwerengero odwala kolera chizikwera. Koma bungwe la United Nations Children’s Fund (Unicef)…
Read More »