Chichewa
-
Bajeti ya chaka chino yavomerezedwa
Nyumba ya Malamulo yavomereza bajeti ya ndalama zokwana K5.998 thililiyoni yoti boma ligwiritse ntchito kuyambira pa 1 April 2024 mpaka…
Read More » -
Dikirani kauniuni wachiwiri wa mbewu
Unduna wa za malimidwe wati anthu asathyolere khosi zotsatira za kauniuni woyamba wa mbewu chifukwa kauniyo sadalingalire za ng’amba yomwe…
Read More » -
Sakufuna awakanize kuima
Mamembala ena a chipani cha Malawi Congress (MCP) akutsutsana ndi maganizo amene komiti yaikulu ya chipanicho (NEC) idamanga kumsonkhano wake.…
Read More » -
Anjata wofuna kugulitsa mwana wake
A Chimwemwe Zololo atha masiku 6 m’chitokosi cha apolisi ku Zomba powaganizira kuti amafuna kugulitsa mwana wompeza. A Zololo akuyembekezereka…
Read More » -
Wa zaka 15 amuganizira kupha mchemwali wa 26
Mwana wa zaka 15 ali m’manja mwa apolisi ku Mangochi pomuganizira kuti adazimitsa mchemwali wake wa zaka 26 pa mkangano…
Read More » -
Ululu podula cha unzika
Walira mvula waliranso matope. Anthu amene amalakalaka atapeza chiphaso cha unzika mwayi wawagwera koma ayenera akhetse thukuta kuti izi zitheke.…
Read More » -
A Chakwera alephera kukwaniritsa lamulo lawo lomwe
Akatswiri pa nkhani za chuma ndi ufulu wa anthu adzudzula mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera kaamba kolephera kukwaniritsa…
Read More » -
Aonjezera aphungu
Bungwe loyendetsa zisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) latsutsa mphekesera yoti layamba laimika kaye chilinganizo choonjezera madera a aphungu pa…
Read More » -
Msungwana adakokera boma kukhoti
Chaka cha 2023 chikupita ndi nkhani zake, imodzi mwa nkhani zimene zidayala nthenje ndi ya msungwana wa zaka 14 yemwe…
Read More » -
Mfumukazi ichereza mayi wobereka ana 5 pa kamodzi
Mkazi wa Inkosi ya Makhosi Gomani V, Inkosikati Rishaladza Khanyisa Gomani wati kuchuluka kwa mimba za ana achichepere kukukolezera kusachita…
Read More »