Chichewa
-
Ana akagonana azimangidwa?
Bwalo lalikulu la milandu Lachitatu likudzali likhala likumva mlandu umene mnyamata wina wa zaka 15 (sitimutchula dzina) wasumira boma. Mnyamatayo…
Read More » -
Esiteti, anthu ayanjana pa za malo
Esiteti ya Lujeri yalola anthu pafupifupi 5 000 amene adalowerera malo a esitetiyo ku Mulanje kuyambira zaka za m’ma 2000…
Read More » -
Apolisi azilembanso mayeso a malamulo
Patadutsa zaka 20 apolisi asakulemba mayeso okhudza zomwe malamulo a ntchito yawo amanena omwe m’Chingerezi amatchedwa Service Standing Order (SSO),…
Read More » -
Apempha alembe aphunzitsi ena
Kadaulo pa za maphunziro a Benedicto Kondowe wati boma likusempha chisa popitiriza kusula aphunzitsi pomwe aphunzitsi ena oposa 9 000…
Read More » -
Magulu othandiza odwala edzi akufa
Chitsime chidauma! Moti magulu 132 mwa 150 olimbana ndi mlili wa edzi mu mzinda wa Mzuzu afa pamene ena 18…
Read More » -
Akana tsankho pa maphunziro
Ophunzira olumala apitirira kukumana ndi mavuto kaamba koti apatsidwa ndalama zochepa mu bajeti ya 2021/22 poyerekeza ndi alunga. Gulu la…
Read More » -
Nkhukutembo ndi dilu
Amaweta nkhukutembo mofanana ndi nkhuku pozipatsa madeya ndi ndiwo zamasamba komanso madzi. Makola nawo ndi osasiyana ndipo zimatha kugonera m’khola…
Read More » -
Wogwira ‘kumaso’ kwa mchemwali wake achimina
Bambo wina wa zaka 32 ku Salima akunong’oneza bondo pano kaamba kosaugwira mtima mpaka kufuna kugonana ndi mchemwali wake. Nkhaniyo…
Read More » -
Akapizana madzi amoto poganizirana miseche
Mayi wa zaka 21 Tionge Gerald ku Mponela m’boma la Dowa wakapiza madzi a moto mkazi mzake Lydia Tembo wa…
Read More » -
‘Boma litisamale pa nkhani ya malo’
Alimi ena ang’onoang’ono m’maboma a Mulanje komanso Thyolo achenjeza boma kuti lisanyozere madandaulo awo akusowa kwa malo ponena kuti maesiteti…
Read More »