Nkhani
-
Kutentha kwa mnanu kunkira
Nthambi ya za nyengo ya Department of Climate Change and Meteorological Services (DCCMS) yati kutentha kwa mnanu komwe kwakhala kuoneka…
Read More » -
Unicef ilipilira asungwana 5 600 fizi
Asungwana 5 600 omwe akadalephera sukulu kaamba ka vuto la fizi achita mwayi ndi lonjezo la bungwe la United Nations…
Read More » -
Mkonono wanyanya kotsutsa
Akadaulo pa nkhani zosiyanasiyana m’dziko muno ati mbali yotsutsa boma ili ndi benthu lake pa mavuto omwe Amalawi akudutsamo chifukwa…
Read More » -
Amanga mbusa wofuna kupumira pa mwana
Khoti la majisitileti m’boma la Dowa lamanga mbusa wina Bonwell Sinoya wa zaka 36 kukagwira ntchito yakalavula gaga kwa zaka…
Read More » -
Malawi wauma
Vuto la mafuta a galimoto lomwe lanyanya tsopano lakweza mkwiyo mwa Amalawi kaamba kakukwera kwa mtengo wa galimoto zonyamula anthu…
Read More » -
Ulendo wotsiriza wa a John Tembo
Thupi la mphangala pa ndale a John Tembo lidalowa m’manda Lachitatu ku mudzi kwawo kwa Kaphala kwa T/A Kachere ku…
Read More » -
Ma rodibuloku abwerere
Kadaulo pa za chitetezo a Loti Dzonzi omwe adakhalako mkulu wa apolisi ( I G ) m’dziko muno waunikira kuti…
Read More » -
A Tembo asiya Amalawi m’misozi
Imfa ya mphangala ya ndale a John Zenus Ungapake Tembo yaonetsa kuti Amalawi ndi amodzi ngakhale kusiyana kwa zipani za…
Read More » -
Liwu la mafumu pa zochotsa anthu 1 miliyoni mu AIP
Mafumu apereka maganizo osiyanasiyana pa ganizo la boma lochotsa maina 1 miliyoni mu pulogalamu ya zipangizo za ulimi zotsika mtengo…
Read More » -
Boma likugwiritsa K3 biliyoni pothandiza ochotsa mimba
Dziko la Malawi likugwiritsa ntchito pafupifupi K3 biliyoni pa chaka popereka thandizo kwa amayi amene anachotsa mimba pogwiritsa ntchito njira…
Read More »