Chichewa
-
Akhazikitsa ndondomeko zoletsaandale kukopa ovota ndi katundu
Mkulu wa ofesi yoona m’mene zipani za ndale zimagwirira ntchito zawo, a Kizito Tenthani, akhala akukumana ndi atsogoleri a zipani…
Read More » -
Achinyamata akufuna maudindo
Mtsogoleri wa bungwe la Youth and Society a Charles Kajoloweka asindika kufunika kokhazikitsa malamulo okakamiza boma kuti lizipereka maudindo ena…
Read More » -
Women yakhazikitsa manifesito
Akatswiri omenyera ufulu wa amayi akuti manifesito ya amayi ndi chida cha mphamvu chosinthira moyo wawo pa ndale m’dziko muno.…
Read More » -
Kuunika za Simatimatiki
Mtsutso wabuka pakati pa zipani zotsutsa boma ndi bungwe loyendetsa zisankho m’dziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) pa nkhani…
Read More » -
Apolisi akonzeka kuthanandi ziwawa zokhudza ndale
KANDANI NGWIRA ndi BRIGHT KUMWENDA Apolisi akuti apereka chitetezo chokwanira m’misonkhano yokopa anthu, povota komanso potulutsa zotsatira za chisankho cha…
Read More » -
Wakuba ufa ndi makala agamulidwa zaka 4
Bambo Cosmas Chiwambo, a zaka 22, omwe amachokera m’mudzi mwa Mwamadi kwa T/A Chikumbu m’boma la Mulanje, alamulidwa kuti akakhale…
Read More » -
Amanga oba zitsulo pa mlatho
Apolisi m’boma la Mulanje atsekera m’chitokosi abambo anayi powaganizira kuti adaba zitsulo za pa mlatho wopezeka m’dera la kummwera cha…
Read More » -
Akachasu nawo akulira ndi kukwera kwa shuga
Mwina n’kumaona ngati amene amakonda za tseketseke monga tiyi ndi makeke okha ndi amene akulira ndi kusowa komanso kukwera mtengo…
Read More » -
Kusamvana pa mwambo wokumbukira Chilima
Mwambo wokumbukira yemwe adali mtsogoleri wakale wa dziko lino a Saulos Chilima uchitika Lachiwiri likudzali kwawo ku Nsipe komwe thupi…
Read More » -
Awachotsa pa mpando atayendera a Bushiri
Kadaulo pa ndale kuno ku Malawi a George Chaima komanso wa ku South Africa a Dr Zwakala ati payenera kukhala…
Read More »