Nkhani
-
Amanga 10 pa mkangano wa ufumu
Apolisi ku Ntchisi amanga anthu 10 a m’mudzi mwa Kanyenda kwa T/A Kalumo potsatira mkangano wa ufumu pakati pa a…
Read More » -
Mitala iphetsa
Mayi wa zaka 19 wadzipha ku Kasungu atazindikira kuti mwamuna yemwe adakwatirana naye pokhulupirira kuti banja lake loyamba lidatha ndi…
Read More » -
Chiyembekezo chakwera ndi mawu a Chakwera
Pakati pa usiku wa Lachitatu sabata yatha, ndalama ya kwacha idatsika mphamvu ndi K44 pa K100 iliyonse. Izi zachititsa kuti…
Read More » -
chiwanda chophana chavuta
Chiwanda chachilendo chophana m’mabanja chalowerera moti mwezi umodzi okha, bambo wina ku Zomba adapha mkazi wake, banja lina ku Chiradzulu…
Read More » -
Kutentha kwa mnanu kunkira
Nthambi ya za nyengo ya Department of Climate Change and Meteorological Services (DCCMS) yati kutentha kwa mnanu komwe kwakhala kuoneka…
Read More » -
Unicef ilipilira asungwana 5 600 fizi
Asungwana 5 600 omwe akadalephera sukulu kaamba ka vuto la fizi achita mwayi ndi lonjezo la bungwe la United Nations…
Read More » -
Mkonono wanyanya kotsutsa
Akadaulo pa nkhani zosiyanasiyana m’dziko muno ati mbali yotsutsa boma ili ndi benthu lake pa mavuto omwe Amalawi akudutsamo chifukwa…
Read More » -
Amanga mbusa wofuna kupumira pa mwana
Khoti la majisitileti m’boma la Dowa lamanga mbusa wina Bonwell Sinoya wa zaka 36 kukagwira ntchito yakalavula gaga kwa zaka…
Read More » -
Malawi wauma
Vuto la mafuta a galimoto lomwe lanyanya tsopano lakweza mkwiyo mwa Amalawi kaamba kakukwera kwa mtengo wa galimoto zonyamula anthu…
Read More » -
Ulendo wotsiriza wa a John Tembo
Thupi la mphangala pa ndale a John Tembo lidalowa m’manda Lachitatu ku mudzi kwawo kwa Kaphala kwa T/A Kachere ku…
Read More »