Chichewa
-
Banja ndalilephera
Anatche, muli bwanji? Ine mavuto.Banja ndidalikondetsetsa koma ndikuona ngati ndililephera. Ndili pa banja ndipo tili ndi ana awiri. Wina wamaliza…
Read More » -
Achenjeza obwereketsa galimoto: Kuli mbanda
Bambo wina yemwe dzina lake ndi Emmanuel Davie, ali m’manja mwa apolisi pomuganizira kuti adanamiza anthu kuti ndi msilikali wa…
Read More » -
‘Smartmatic’ yautsa mapiri pa chigwa
Njira yamakina a makono oyendetsera zisankho otchedw Elections Monitoring Devices (EMD) amene akutchuka ndi dzina la kampani yak u Netherlands…
Read More » -
Polisi yati mitima ikhale mmalo
Mkulu wa apolisi Mayi Me r l y ne Yol amu atsimikizira zipani za ndale ndi mabungwe oima paokha kuti…
Read More » -
DPP, MCP alozana zala
Zipani za MCP ndi DPP zikulozana zala pa amene adayambitsa ziwawa zimene zidachitika ku mapeto a sabata yatha ku Mponela…
Read More » -
Thandizo sakakamiza, watero Namadingo
Pomwe chiyembekezo cha mafumu cha anthu a ku Mangochi chili mmwamba kuti maambulansi amene adafa ndipo woimba Patience Namadingo anadzipereka…
Read More » -
‘Dekhani za a bushiri’
Oimira anthu pa milandu, a Jai Banda komanso a Khwima Mchizi apempha Amalawi kuti adekhe pa mlandu omwe mneneri wa…
Read More » -
Aotcha makilogalamu a chamba
Bwalo la milandu ku Salima lagamula kutentha chamba chokwana makilogalamu 576.68 komanso kuti mwini wake, a Adam Likagwa a zaka…
Read More » -
Apempha zipani kuthandiza a ulumali
Mkulu wa bungwe la Disability HIV/Aids Trust yomwe ndi nthambi ya Federation of Disability Organizations in Malawi (Fedoma) a David…
Read More » -
Kwadza zipani zina za ndale
Pomwe masiku a chisankho akusunthira ku chitseko, zipani zina za ndale zitatu zalembetsa ku ofesi ya mlembi wa zipani za…
Read More »