Chichewa
-
Apempha zipani kuthandiza a ulumali
Mkulu wa bungwe la Disability HIV/Aids Trust yomwe ndi nthambi ya Federation of Disability Organizations in Malawi (Fedoma) a David…
Read More » -
Kwadza zipani zina za ndale
Pomwe masiku a chisankho akusunthira ku chitseko, zipani zina za ndale zitatu zalembetsa ku ofesi ya mlembi wa zipani za…
Read More » -
Ena ayamba kukolola chimanga chosauma
Mbala zavuta mpaka alimi ena ayamba kukolola dowe kuopa kuti akadikira nyengo yoyenera kukolola adzapeza mapesi okhaokha m’munda. Nduna ya…
Read More » -
Dausi aseketsa aphungu
Zitsuzo sizimamuthera phungu wa m’dera lapakati m’boma la Mwanza a Nicholas Dausi. A Dausi adadzuka pa mpando wawo m’Nyumba ya…
Read More » -
Anthu alembetsa mwaunyinji—MEC
Bungwe loyendetsa zisankho la MEC lati anthu chiwerengero cha anthu omwe alembetsa kuti adzavote pa Chisankho Chachikulu cha pa 16…
Read More » -
Amuna anga matama thooo!
Azakhali, zili kwathu simungazimvetse. Ife tonse tili pa ntchito. Tonse timalandira ndalama zokwanira ndithu. Komwe ndalama za amuna anga zimapita…
Read More » -
‘Samalani m’masamba a mchezo’
Mkulu wa bungwe loteteza ufulu wa ana ndi achinyamata a MacBain Mkandawire wapempha Amalawi kuti azigwiritsa ntchito masamba a mchezo…
Read More » -
America iyimika thandizo
Kadaulo wa mgwirizano wa mabungwe a zaumoyo la Malawi Health Equity Network (Mhen) a George Jobe ati zomwe lachita dziko…
Read More » -
Mtengo wa chimanga wapenga
Kusowa kwa chimanga m’misika ya Admarc kwapereka danga kwa mavenda ogulitsa chimangacho kuti akame Amalawi omwe akulira kale ndi njala…
Read More » -
Ati tikhwimire mwana
Ndili pa banja ndipo tili ndi ana angapo. Banja lathu ndi loopa Mulungu. Ndipo tonse ndi atsogoleri ku mpingo wathu.…
Read More »