Chichewa
-
NRB ilembere opanda ma ID
Pamene kalembera wa amene akufuna kudzavota pa Chisankho Chachikulu cha pa 16 September chaka cha mawa ali mkati, anthu amene…
Read More » -
A Kaliati akadali m’manja mwa apolisi
Mlembi wamkulu wa chipani cha UTM mayi Patricia Kaliati akhoza kukhala m’chitokosi ku mapeto kwa sabata ino m’chitokosi kuchokera pomwe…
Read More » -
Ndidatseketsa mowabisira
Azakhali, Mutu wanga waima chifukwa ndazunguzika ndi mavuto omwe ndikukumana nawo. Ine ndi mayi wa ana atatu ndipo ndili pa…
Read More » -
Kalembera wa chisankho ayamba lolemba lomweli
Kalembera wa chisankho cha 2025 ayamba Lolemba likudzali pomwe zipani zakangalika kumema anthu ozitsatira kuti akalembetse mwa unyinji kuti adzakhale…
Read More » -
Kamangila wakwekwesa jaji
Woweruza milandu ku khoti la za chuma a Kenan Manda ati mmodzi mwa maloya odziwika a Alexious Kamangila awapepese kaamba…
Read More » -
A ‘blesser’ andipatsa mimba
Anatchereza, Ndili ndi zaka 22 ndipo ndili ku sukulu ya ukachenjedwe chaka chachiwiri. Ine ndi wochokera banja losauka kwambiri. Makolo…
Read More » -
Amanga mbusa wogwirira mwana
Apolisi m’boma la Chiradzulu Lachinayi adamanga mbusa wina wa zaka 35 pomuganizira kuti anagwirira mwana wa zaka 16 yemwe ndi…
Read More » -
Mayi adzipha ku Mulanje
Mayi wina wa zaka 29 wadzikhweza ndi nsalu ku denga la nyumba yake pa zifukwa zomwe sizikudziwika ku Mulanje. Wachiwiri…
Read More » -
MEC yakhazikika pa cha unzika pa kalembera
Bungwe loyendetsa zisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) latemetsa nkhwangwa pa mwala kuti ligwiritsabe ntchito chiphaso cha unzika ngati chizindikiro…
Read More » -
Mabungwe akufuna lamulo loletsa ziponda ku ndale
Mabungwe okhudzidwa ndi kayendetsedwe ka zisankho ati lamulo loletsa kugawa zinthu kwa anthu ngati njira yowakopera pa ndale (ena amati…
Read More »